Mawu a M'munsi
a Josephus akusimba kuti Aroma oukirawo anazinga mzindawo, kukumba mbali ina ya khomalo, ndipo anali pafupi kuyatsa moto chipata cha kukachisi wa Yehova. Ayuda otsekeredwa mkati anachita mantha kwambiri ndi zimenezi, popeza kuti anaona imfa ikuyandikira.—Wars of the Jews, Book II, mutu 19.