Mawu a M'munsi
a Mtengo wa “ndalama” iliyonse (m’Chihebri, qesi·tahʹ) sudziŵika bwino. Koma m’tsiku la Yakobo anthu anali kugula malo aakulu ndithu ndi “ndalama zana” limodzi. (Yoswa 24:32) Choncho, “ndalama” imodzi yochokera kwa mlendo aliyense mwinamwake inali mphatso yaikulu ndithu.