Mawu a M'munsi
b Nyumba zina za alendo za m’tsiku la Yesu mwachionekere sizinali kupereka chabe malo ogona komanso chakudya ndi zinthu zina. Mwina umenewu ndiwo umene unali mtundu wa nyumba zimene Yesu anali kulingalira, popeza kuti mawu achigiriki ogwiritsiridwa ntchito panopo ngosiyana ndi amene anatembenuzidwa kuti “nyumba ya alendo” pa Luka 2:7.