Mawu a M'munsi
a “Maziko a dziko” angatanthauze mphamvu zachilengedwe zimene zimaligwira—ndi zakumwamba zonse—kuti likhazikike zolimba. Ndiponso, dziko lapansi linamangidwa mwanjira yakuti “silidzagwedezeka” konse, kapena kuwonongeka.—Salmo 104:5.