Mawu a M'munsi
c Paulo anali kukayikira chipulumutso cha “ntchito” ya womangidwayo, osati cha womangayo ayi. The New English Bible imati pavesili: “Ngati nyumba ya munthu iima, adzafupidwa; ngati itenthedwa, adzatayikidwa; komano adzapulumutsa moyo wake, monga momwe munthu angaupulumutsire ku moto.”