Mawu a M'munsi
b Zinthu zinakhaladi choncho kuti matembenuzidwe a Jerome anakhala Baibulo logwiritsidwa ntchito kwambiri m’Dziko Lachikristu la Kumadzulo, pamene Septuagint ndi imene idakali kugwiritsidwa ntchito m’Dziko Lachikristu la Kummaŵa lerolino.