Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c M’buku lakuti History of the Jews, Polofesa Graetz ananena kuti nthaŵi zina Aroma anali kupachika akaidi 500 patsiku. Ayuda ena amene anatengedwa ukapolo anadulidwa manja kenako n’kuwabwezera kumzindawo. Kodi moyo unali wotani kumeneko? “Ndalama inatheratu mphamvu, popeza sinalinso kugula mkate. Amuna m’misewu anali kumenyanirana chakudya chonyansa kwadzaoneni, timapesi touma, kachikopa, kapena matumbo otayidwa kuti agalu adye. . . . Kuwonjezeka kwakukulu kwa mitembo yosaikidwa m’manda kunapangitsa mpweya wotentha wa m’chilimwewo kukhala ngati mliri, ndipo anthu ambiri anafa ndi matenda, njala, ndi lupanga.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena