Mawu a M'munsi
c Buku lotchedwa Word Origins (Chiyambi cha Mawu) la Wilfred Funk limati: “Agiriki anali kunyoza zinenero za anthu ena, ndipo anali kunena kuti amamveka ngati akuti ‘bar-bar’ ndipo aliyense amene anali kuyankhula zinenero zoterozo anali kumutcha kuti barbaros.”