Mawu a M'munsi
a M. J. Gruenthaner, Mjezwiti yemwe ndi katswiri wamaphunziro, pamene anali mkonzi wamkulu wa magazini yotchedwa The Catholic Biblical Quarterly, anafotokoza mneni ameneyu malinga ndi mmene anafotokozera mneni wina wofanana naye, kuti “sanena za chinthu chosadziŵika bwino chimene munthu amangoyerekeza kuti chilipo koma nthaŵi zonse amanena za chinthu chenicheni chokhalako, kutanthauza kuti choonekera m’njira yozindikirika bwino kuti chilipodi.”