Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a M. J. Gruenthaner, Mjezwiti yemwe ndi katswiri wamaphunziro, pamene anali mkonzi wamkulu wa magazini yotchedwa The Catholic Biblical Quarterly, anafotokoza mneni ameneyu malinga ndi mmene anafotokozera mneni wina wofanana naye, kuti “sanena za chinthu chosadziŵika bwino chimene munthu amangoyerekeza kuti chilipo koma nthaŵi zonse amanena za chinthu chenicheni chokhalako, kutanthauza kuti choonekera m’njira yozindikirika bwino kuti chilipodi.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena