Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Buku lotchedwa Cyclopedia lolembedwa ndi McClintock ndi Strong limati: “Amsonkho otchulidwa m’Chipangano Chatsopano ankaonedwa monga akapirikoni ndi am’patuko, odetsedwa chifukwa cha kuyanjana kwawo nthaŵi zonse ndi anthu akunja, pokhala ziŵiya za opondereza. Anali kuwaika m’gulu limodzi ndi ochimwa . . . Posankhulidwa chotero ndiponso kupeŵedwa ndi anthu a moyo wabwino, mabwenzi awo okha kapena anzawo anali kupezeka pakati pa awo amene anali anthu okanidwa ofanana ndi iwo.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena