Mawu a M'munsi
b Milandu ina ya chinyengo, bodza, kapena ukathyali m’nkhani zabizinesi kapena zandalama ingaphatikizidwe pa machimo amene Yesu anatanthauza. Chosonyeza zimenezo n’chakuti atapereka malangizo olembedwa pa Mateyu 18:15-17, Yesu anapereka fanizo la akapolo (antchito) amene anakongola ndalama nalephera kuzibweza.