Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

f M’fanizo la nkhosa ndi mbuzi, Mwana wa munthu akufika muulemerero wake panthaŵi ya chisautso chachikulu nakhala pansi kuti apereke chiweruzo. Akuweruza anthu pamaziko akuti kaya anachirikiza abale a Kristu odzozedwa kapena ayi. Maziko oweruzirapo anthu ameneŵa angakhale opanda pake zitakhala kuti podzafika nthaŵi yachiweruzoyo, abale onse a Kristu adzakhala kuti anachokapo kalekale padziko lapansi.​—Mateyu 25:31-46.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena