Mawu a M'munsi
a Malinga n’kunena kwa buku lotchedwa The New Brown-Driver-Briggs-Gesenius Hebrew and English Lexicon, m’nkhani imeneyi mawu achihebri akuti chen, otembenuzidwa kuti “chosiririka,” amatanthauza ‘maonekedwe ndi kaumbidwe ka thupi kochititsa kaso kapena kokongola.’