Mawu a M'munsi
b Pa Machitidwe 13:2, pakusimba kuti aneneri ndi aphunzitsi ku Antiokeya anali “kutumikira” Yehova [“kuchita utumiki wothandiza anthu kwa Yehova,” NW] (kutembenuza mawu achigiriki ofanana ndi lei·tour·giʹa). Utumiki wothandiza anthu umenewu uyenera kuti unaphatikizapo kulalikira kwa anthu.