Mawu a M'munsi
b Ngakhale kuti Aroma 12:1 kwenikweni amanena za Akristu odzozedwa, mfundo yakeyo imakhudzanso “nkhosa zina.” (Yohane 10:16) Ameneŵa “adziphatika okha kwa Yehova, kuti am’tumikire Iye, ndi kukonda dzina la Yehova, akhale atumiki ake.”—Yesaya 56:6.