Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Polalikira Ufumu wa Mulungu, Mboni za Yehova siziloŵerera m’nkhani zandale kapena kupanga magulu oukira boma ngakhale m’mayiko omwe amaziletsa kapena kuzizunza. (Tito 3:1) M’malo mwake, zimayesetsa mosaloŵetsapo ndale kuthandiza mwauzimu monga momwe Yesu ndi ophunzira ake anachitira. Mboni zimayesetsa kuthandiza anthu oona mtima m’madera osiyanasiyana omwe zimakhala kuti aphunzire makhalidwe abwino a m’Baibulo monga chikondi cha pa banja, kuona mtima, kudzisunga, ndiponso makhalidwe abwino a ku ntchito. Kwenikweni, Mboni zimayesetsa kuphunzitsa anthu mmene angatsatirire mfundo zachikhalidwe za m’Baibulo ndiponso kuti aziyembekezera Ufumu wa Mulungu wokha kuti ndiwo udzathetse mavuto a anthu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena