Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Akatswiri ena amakonda kugwiritsa ntchito dzina lakuti “Yahweh” m’malo mwa “Yehova.” Ngakhale zili choncho, otembenuza mabaibulo amakono ambiri achotsa dzina la Mulungu m’mabaibulo awo, ndi kuikamo mayina aulemu omwe angaperekedwe kwa aliyense monga “Ambuye” kapena “Mulungu.” Kuti mudziŵe zambiri zokhudza dzina la Mulungu, onani buku lakuti Dzina la Mulungu Limene Lidzakhala Kosatha, lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena