Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Anzake a Kora achiwembu, Datani ndi Abiramu, anali a fuko la Rubeni. Choncho, mwachionekere iwo sanali kufuna ntchito ya unsembe. M’malo mwake iwo anali kuipidwa ndi utsogoleri wa Mose ndiponso kuti mpaka pa nthaŵi imeneyo, anali asanaloŵebe m’Dziko Lolonjezedwa limene anali kuliyembekezera.​—Numeri 16:12-14.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena