Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c M’nthaŵi za makolo akale, mwamuna aliyense anali kuimira mkazi wake ndi ana ake kwa Mulungu, ngakhalenso kupereka nsembe m’malo mwawo. (Genesis 8:20; 46:1; Yobu 1:5) Komabe, atakhazikitsa Chilamulo, Yehova anaika amuna a m’banja la Aroni kukhala ansembe kuti nsembe ziziperekedwa kudzera mwa iwo. Anthu oukira 250 amenewo mwachionekere sanafune kutsatira kusintha kwa zinthu kumeneku.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena