Mawu a M'munsi
a Yehova atasankha Mose ndi Aroni kuti akalankhule ndi Farao m’malo mwa anthu ake, Iye anauza Mose kuti: ‘Ndakuika ngati Mulungu kwa Farao; ndi Aroni mkulu wako adzakhala mneneri wako.’ (Eksodo 7:1) Aroni anali mneneri mulingaliro lakuti anali wom’lankhulira Mose osati wolosera za m’tsogolo.