Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a M’kalata imene analemba pa November 20, 1861, yopita komwe amapanga ndalama zachitsulo ku United States, Nduna ya Zachuma a Salmon P. Chase anati: “Kuti dziko likhale lamphamvu liyenera kudalira mphamvu za Mulungu, ndipo lingakhale lotetezeka ngati Iye aliteteza. Anthu athu amakhulupirira Mulungu ndipo tiyenera kusonyeza zimenezi pa ndalama zachitsulo za dziko lathu.” Chifukwa cha zimenezi, mu 1864 anayamba kulemba mawu akuti “Timakhulupirira Mulungu” pa ndalama zachitsulo za ku United States.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena