Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Pa chibowo cha Rano Raraku chimene chinkatuluka chiphalaphala pali ziboliboli zambiri. Mpikisano wa anthu ofuna kulamulira pachilumbachi unkayambira pa Rano Kau. Anali kuchita mpikisano wotsika pamalo okwera kwambiri, kusambira kupita pa zilumba zina zazing’ono, kukatenga dzira la mbalame ina yopezeka kumeneko, n’kusambiranso kubwerera pachilumba chija, n’kukweranso pamalo okwera kwambiri aja dzira lili losasweka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena