Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Panthaŵi ina Paulo ndi Akristu ena anayi anapita kukachisi kukadziyeretsa mwamwambo. Nthaŵiyi n’kuti Chilamulo chitatha ntchito, komabe Paulo anachita izi potsatira malangizo a amuna akulu a ku Yerusalemu. (Machitidwe 21:23-25) Koma n’kutheka kuti Akristu ena anaganiza kuti iwo sakanaloŵa m’kachisi kapena kuchita mwambo umenewo. Panthaŵiyo anthu anali ndi chikumbumtima chosiyanasiyana, ndipo ndi mmenenso zilili masiku ano.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena