Mawu a M'munsi
b Mavesi ena a Malemba Achigiriki Achikristu amasonyezanso kuti Yesu ndiye Wodzozedwa wa Mulungu wotchulidwa m’salmo lachiŵirili. Timaona zimenezi tikayerekezera Salmo 2:7 ndi Machitidwe 13:32, 33 komanso tikaliyerekezera ndi Ahebri 1:5; 5:5. Onaninso Salmo 2:9 ndi Chivumbulutso 2:27.