Mawu a M'munsi
a Iliyonse ya mfundo zimene Yesu ananenazi imayamba ndi mawu achigiriki oti ma·kaʹri·oi. M’malo momasulira mawu ameneŵa kuti “odala,” ngati mmene mabaibulo ena amachitira, Baibulo la New World Translation ndi mabaibulo ena, monga The Jerusalem Bible ndi Today’s English Version, amawamasulira molondola kuposa pamenepo kuti “achimwemwe.”