Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zinali kwa munthu amene akulumbirayo kudzisankhira kutalika kwa nthawi yomwe akufuna kukhala Mnaziri. Koma, malinga ndi nkhani zakale za Ayuda, nthawi yomwe munthu angakhale Mnaziri inkayambira pa masiku 30. Ankaganiza kuti kupanga lumbiro la masiku osakwana 30 kukanachitititsa kuti lumbiroli lingokhala ngati lumbiro wamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena