Mawu a M'munsi
a Abrahamu anali ndi chifukwa chomveka chochitira mantha, chifukwa buku lina lakale, limasimba za Farao wina amene anauza asilikali ake kugwira mkazi wokongola, ndi kupha mwamuna wake.
a Abrahamu anali ndi chifukwa chomveka chochitira mantha, chifukwa buku lina lakale, limasimba za Farao wina amene anauza asilikali ake kugwira mkazi wokongola, ndi kupha mwamuna wake.