Mawu a M'munsi
b Mboni za Yehova zimakhala ndi nkhani ya mphindi 30 yakuti “Ukwati Wolemekezeka M’maso mwa Mulungu.” Nkhaniyi imakhala ndi malangizo abwino kwambiri a m’Malemba opezeka m’buku lakuti Chinsinsi cha Chimwemwe cha Banja ndiponso mabuku ena a Mboni za Yehova, ndipo imakhala yothandiza kwambiri anthu omwe akukwatiranawo ndiponso anthu ena onse opezeka pa mwambowo.