Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Anthu amenewa anathandiza kwambiri pamaphunziro a zinenero zimene anthu olemba Baibulo anagwiritsira ntchito. Mu 1506, Reuchlin anafalitsa buku lake la malamulo a chinenero cha Chiheberi. Bukuli linathandiza kuti anthu aphunzire mozama Malemba Achiheberi. Mu 1516, Erasmus anafalitsa Baibulo la Malemba Achigiriki Achikristu popanda kusintha chinenerocho.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena