Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Agiriki ankakonda kwambiri maphunziro apamwamba. Plutarch, amene anakhala ndi moyo nthawi imodzi ndi Timoteyo, analemba kuti: “Maphunziro apamwamba ndi gwero ndi muzu wa zinthu zonse zabwino. . . . Ndi maphunziro amenewa, amene amathandiza munthu kukhala ndi makhalidwe abwino kwambiri komanso chimwemwe. . . . Zinthu zina zonse ndi zopanda phindu ndi zachabechabe ndipo palibe chifukwa chovutikira nazo.”​—Moralia, I, “The Education of Children.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena