Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Jonatani anali wazaka zosachepera 20 pamene anatchulidwa koyamba monga woyang’anira gulu lankhondo, chakumayambiriro kwa ulamuliro wa zaka 40 wa Sauli. (Numeri 1:3; 1 Samueli 13:2) Motero, pamene Jonatani ankamwalira cha m’ma 1078 B.C.E., ayenera kuti anali ndi zaka pafupifupi 60. Popeza kuti panthawiyi Davide anali ndi zaka 30, zikuoneka kuti Jonatani ankasiyana zaka pafupifupi 30 ndi Davide.​—1 Samueli 31:2; 2 Samueli 5:4.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena