Mawu a M'munsi
a Pangano lina limene linapezedwa ku Nuzi, m’dziko la Iraq linati: “Kelim-ninu tam’pereka kwa Shennima kuti akhale mkazi wake. . . . Ngati Kelim-ninu sadzabereka [ana], Kelim-ninu adzakatenge mkazi [mdzakazi] ku dera la Lullu kuti akhale mkazi wa Shennima.”