Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Phiri la Karimeli nthawi zambiri limakhala lobiriwira komanso kumawomba kamphepo kayeziyezi kochokera m’nyanja ndipo zimenezi zimachititsa kuti kawirikawiri kuzigwa mvula ndi mame ambiri. Chifukwa chakuti anthu ankanena kuti Baala ndi amene amabweretsa mvula, mwachionekere phiri limeneli ndi limene linali malo ofunika kwambiri pa kulambira Baala. Koma panthawiyi zinasonyezeratu kuti Baala ndi mulungu wonyenga chifukwa phiri la Karimeli linauma ndiponso linali lopanda zomera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena