Mawu a M'munsi
a Tanthauzo la pa·rou·siʹa lingadziwike poona kusiyana pakati pa mawu akuti ‘kukhalapo’ kwa mtumwi Paulo ndi akuti “kulibe” opezeka pa 2 Akorinto 10:10, 11 ndi Afilipi 2:12. Kuti mumve zambiri, onani Insight on the Scriptures, Voliyumu 2, masamba 676-679.