Mawu a M'munsi
c Zikuoneka kuti nthawi imene “m’badwo uwu” ulipo ndi imodzimodzi ndi nthawi ya kukwaniritsidwa kwa masomphenya oyamba a m’buku la Chivumbulutso. (Chiv. 1:10–3:22) Mbali imeneyi ya tsiku la Ambuye ikuyambira mu 1914 mpaka tsiku limene wodzozedwa wokhulupirika womaliza adzamwalira ndi kuukitsidwa.—Onani Revelation—Its Grand Climax At Hand! tsamba 24, ndime 4.