Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mtumwi Paulo anagwiritsa ntchito liwu lovuta kulimasulira ndi mawu amodzi. Buku lina limati: “Liwulo limanena za mtima umene umalolera kudzimana ufulu wako ndiponso woganizira ena komanso wachifundo.” Choncho mfundo ya liwulo imaphatikizapo kukhala wololera, osati kuumiriza munthu kuti atsatire malamulo mosaphonyetsako kapena kuumirira kuti ndi ufulu wanga kuchita zakutizakuti.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena