Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Mawu a Chiheberi akuti “nsomba,” m’Chigiriki anawamasulira kuti “chilombo cha m’nyanja,” kapena “chinsomba chachikulu.” Sitingathe kudziwa kuti imeneyi inali nsomba yamtundu wanji kwenikweni, komabe tikudziwa kuti m’nyanja ya Mediterranean muli nsomba zikuluzikulu zotchedwa shaki zimene zingathe kumeza munthu wathunthu. M’nyanja zina nsomba zimenezi zimatha kukula kwambiri moti zina zimakhala zazitali mamita 15, kapenanso kuposa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena