Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Magazi, omwe Mulungu amawaona kuti ndi opatulika, ndi omwe ankathandiza kuti iye akhululukire munthu machimo ake. (Levitiko 17:11) Ndiyeno kodi zimenezi zikusonyeza kuti nsembe za ufa zimene anthu osauka ankapereka zinali zopanda ntchito? Ayi, chifukwa Yehova ankaona kuti anthu omwe ankapereka nsembe zotere ankasonyeza kudzichepetsa komanso kumvera. Ndiponso machimo a Aisiraeli onse, kuphatikizapo omwe anali osauka, ankakhululukidwa chifukwa cha magazi a nyama zomwe zinkaperekedwa nsembe kwa Mulungu chaka chilichonse pa Tsiku la Chitetezo.​—Levitiko 16:29, 30.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena