Mawu a M'munsi
c Mawu omwe mnyamatayo anagwiritsira ntchito ponena za Nabala amatanthauzanso kuti “mwana wa beliyali (wachabechabe).” Pavesi limeneli, mabaibulo ena amati Nabala anali “munthu wosamva za ena,” ndipo “sichinali chinthu chanzeru kulankhula naye.”