Mawu a M'munsi
a Zikuoneka kuti mtumwi Petulo anasamukira ku Kaperenao kuchoka ku Betsaida kuti azikagwira ntchito yopha nsomba ndi mchimwene wake Andireya komanso ana a Zebedayo. Yesu anakhalanso ku Kaperenao kwa kanthawi ndithu.—Mateyo 4:13-16.
a Zikuoneka kuti mtumwi Petulo anasamukira ku Kaperenao kuchoka ku Betsaida kuti azikagwira ntchito yopha nsomba ndi mchimwene wake Andireya komanso ana a Zebedayo. Yesu anakhalanso ku Kaperenao kwa kanthawi ndithu.—Mateyo 4:13-16.