Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Taonani ena mwa malonjezo amene Yoswa anaona akukwaniritsidwa. Yehova adzapatsa Aisiraeli dziko lawolawo. (Yerekezerani Genesis 12:7 ndi Yoswa 11:23.) Yehova adzalanditsa Aisiraeli m’dziko la Iguputo. (Yerekezerani Eksodo 3:8 ndi Eksodo 12:29-32.) Yehova adzasamalira anthu ake.​—Yerekezerani Eksodo 16:4, 13-15 ndi Deuteronomo 8:3, 4.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena