Mawu a M'munsi
a “Nkhosa zina” za Yesu zidzakhala ana a Mulungu pamapeto pa zaka 1,000. Komabe, chifukwa choti iwowa anadzipereka kwa Mulungu, angathe kutchula Mulungu kuti “Atate” ndipo amaonedwa kuti ali m’banja la olambira Yehova.—Yoh. 10:16; Yes. 64:8; Mat. 6:9; Chiv. 20:5.