Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Mateyo analemba kuti alendo amenewa “anamasula chuma chawo” ndipo anam’patsa Yesu golide, lubani ndi mule. N’zochititsa chidwi kuti mphatso zamtengo wapatali zimenezi zinafika panthawi yake, popeza zikuoneka kuti makolo a Yesu anali osauka ndiponso chifukwa choti anali atatsala pang’ono kuthawira kudziko lina.​—Mateyo 2:11-15.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena