Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Ngakhale kuti Baibulo limanena kuti Yehova ‘anatseka mimba ya Hana,’ palibe umboni wosonyeza kuti Mulungu sankasangalala ndi Hana, yemwe anali mkazi wokhulupirika komanso wodzichepetsa. (1 Samueli 1:5) Baibulo nthawi zina limanena kuti Mulungu wachititsa chinachake, koma kwenikweni amakhala kuti wangolola kuti zichitike.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena