Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Pamenepa, Petulo sanali kunena za dziko lapansi lenilenili. Mose, yemwe analemba nawo Baibulo, anagwiritsanso ntchito mawu akuti “dziko lapansi” mophiphiritsa. Iye anati: “Dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi.” (Genesis 11:1) Dziko lapansi lenilenili si limene limalankhula “chinenedwe chimodzi.” Mofananamo, si dziko lenilenili limene lidzawonongedwe. M’malo mwake, mogwirizana ndi zimene Petulo ananena, amene adzawonongedwe ndi anthu osaopa Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena