Mawu a M'munsi
a Pa lemba la Aheberi 10:5-10, mtumwi Paulo anagwira mawu Salmo 40:6-8 kuchokera m’Baibulo la Greek Septuagint limene lili ndi mawu akuti, “munandikonzera thupi.” Mawu amenewa sapezeka m’mipukutu yakale yomasulira Malemba Achiheberi.
a Pa lemba la Aheberi 10:5-10, mtumwi Paulo anagwira mawu Salmo 40:6-8 kuchokera m’Baibulo la Greek Septuagint limene lili ndi mawu akuti, “munandikonzera thupi.” Mawu amenewa sapezeka m’mipukutu yakale yomasulira Malemba Achiheberi.