Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Nkhani imeneyi imanena zinthu ziwiri zopanda ulemu zimene ana a Eli ankachita. Chilamulo chinaneneratu zigawo za nyama yoperekedwa nsembe zimene ansembe anayenera kudya. (Deuteronomo 18:3) Koma kuchihemako, ansembe oipa amenewo anayamba kuchita zawozawo. Iwo ankauza anthu owathandizira kuti azipisa ndi chifoloko chachikulu m’miphika ya nyama imene inali pamoto ndipo ankatenga nyama iliyonse imene akufuna. Komanso anthu akabweretsa nsembe zawo kuchihema kuti azipereke paguwa la nsembe, ansembe oipawo ankachititsa owathandizira awo kuchitira chipongwe anthu odzapereka nsembewo. Ankachita zimenezi pokakamiza anthu kuti aziwapatsa nyama yosaphika ngakhale asanapereke mafuta a nyamayo ngati nsembe kwa Yehova.​—Levitiko 3:3-5; 1 Samueli 2:13-17.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena