Mawu a M'munsi
a Buku lina limanena kuti mawu a Yobu akuti “mukanandibisa,” ayenera kuti ankatanthauza kuti “munditeteze ngati chuma chamtengo wapatali.” Komanso buku lina limanena kuti pamenepa Yobu ankatanthauza kuti “mundibise ngati chuma chamtengo wapatali.”