Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Azimayi ambiri amavutika maganizo kwa milungu yochepa akangobereka kumene. Koma ena amadwala matenda enaake ovutika maganizo amene azimayi omwe angobereka kumene amadwala. Kuti mudziwe zimene mungachite pofuna kuzindikira komanso kuthana ndi matenda amenewa, werengani nkhani yakuti “Ndinagonjetsa Vuto Langa Losokonezeka Maganizo Nditabereka,” mu Galamukani! ya August 8, 2002, ndi yakuti “Understanding Postpartum Depression,” mu Galamukani! yachingerezi ya June 8, 2003. Magazini amenewa ndi ofalitsidwa ndi Mboni za Yehova. Mungawerengenso nkhani zimenezi m’Chingelezi pa Intaneti pogwiritsa ntchito adiresi iyi, www.jw.org.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena