Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Sikuti mtengo wa maoliviwu poyamba unkaimira mtundu wa Isiraeli. Tikunena choncho chifukwa chakuti mtunduwu sunakhale ufumu wa ansembe, ngakhale kuti Aisiraeli ena anakhala mafumu ndipo ena anali ansembe. Mu Isiraeli, lamulo silinkalola mafumu kukhala ansembe. Choncho mtengo wa maoliviwu sunaimire mtundu wa Isiraeli. Paulo anagwiritsa ntchito fanizoli posonyeza kuti cholinga cha Mulungu choti apange ‘ufumu wa ansembe’ chidzakwaniritsidwa ndi Aisiraeli auzimu. Mfundo imeneyi ikusintha zimene zinalembedwa mu Nsanja ya Olonda ya Chingelezi ya August 15, 1983, tsamba 14 mpaka 19.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena